Phunziro 13 September 26 2020 Kukhazikitsa njira Yesu Chiyambi cha ulendo Petro Yohane Mateyu Kufikira Cholinga Paulo Kuyambiranso ulendo ID: 813187
Download The PPT/PDF document "KUYAMBA ULENDO MU CHIKHULUPIRIRO" is the property of its rightful owner. Permission is granted to download and print the materials on this web site for personal, non-commercial use only, and to display it on your personal computer provided you do not modify the materials and that you retain all copyright notices contained in the materials. By downloading content from our website, you accept the terms of this agreement.
Slide1
KUYAMBA ULENDO MUCHIKHULUPIRIRO
Phunziro
13,
September
26, 2020
Slide2Kukhazikitsa
njira
:
Yesu
Chiyambi cha ulendo: Petro, Yohane, MateyuKufikira Cholinga: PauloKuyambiranso ulendo: Kodi mukonda ine?Njira ya Chikondi: Chimwemwe pa kugawana
Kuyamba kuyenda muchikhulupiriro ndikofunikira kuti tipeze Chimwemwe potenga nawo mbali mu utumiki wo itanira abwenzi kwa Yesu.Yesu anationetsa ife njira kudzera mu chitsanzo chake. Iyi ndi njira yomwe ena anatenga kale.Chimwemwe sichinasungidwe kwa mphotho yomaliridzira yokha, koma chili mbali yaulendo. Timadzadzidwa ndi Chimwemwe tikaona ena akulandira Yesu kukhala mpulumutsi wa moyo wawo.
Slide3KUKHAZIKITSA NJIRA“
Mukhale
nao
mtima m'kati mwanu umene unalinso mwa Khristu Yesu.” (Afilipi 2:5)
Yesu ndi Mulungu, koma anasankha “kusiya” kaye ulemerero wake pamene anasiya mpando wake kumwamba monga mfumu yadziko ndikudzakhala munthu (Afilipi. 2:6-7).Sanababwe ngati munthu otchuka, koma ngati kapolo odzichepetsa. Kuphatikiza pamenepa: Anagonjera kwathunthu chifuniro cha Mulungu, nakhala omvera kufikira imfa ya pa mtanda chifukwa cha chikondi chake
pa ife. (Afilipi. 2:8).
Chifukwa
cha
chikondi
chopanda
undekha ichi, Mulungu “anamukweza, namupatsa dzina limene
liposa maina onse.” (Afilipi. 2:9). Komabe, Chisangalalo chake
chachikulu sichinali kukwezedwako,
koma kuti “Adzaona zotsatira za mavuto a moyo wake nadzakhutitsidwa
nazo.” (Yesaya. 53:11)Pamene tikutsata mayendedwe a
chikhulupiriro a Yesu, Chisangalalo
chathu chachikulu chidzakhala kuona anthu akupereka miyoyo
yawo
kwa
mpulumutsi
,
ndikudzakhala
moyo wamuyaya ndi Yesu.
Slide4CHIYAMBI CHA ULENDO
“
Ndipo
iwo
anasiya pomwepo makokawo, namtsata Iye.” (Mateyu 4:20)Andrea, Petro, Yohane, ndi Yakobo anali atamutsata Yesu kwa kanthawi. Pambuyo
pake, anaitanidwa kuti amutsate “nthawi zonse.” Yesu anawalimbikitsa kuti asiye kukhala asodzi a nsomba nakhala “asodzi a anthu.” (Mateyu. 4:19).Anasiya chirichonse nadzipereka kugawana ndi ena za chikondi cha Yesu.Mateyu analinso munthu wina amene Yesu anamuitana kuti
aleka zina zonse. Yesu anadziwa zokhumba za mtima wake, anamulimbikitsa kusinthitsa moyo
wake ofewa koma osakhutitsidwa ndi moyo
okhala ndi cholinga
ndikukhutitsidwa (Matthew 9:9).
Ifenso, tikufuna kukhala moyo wopindula china chake,
wopambana ndi wokhala nacho
cholinga chabwino, chotero tiyankhe kuitana kwa
Khristu kuti timutsate.
Slide5KUFIKIRA CHOLINGA
“
Ndalimbana
nako
kulimbana kwabwino, ndatsiriza njirayo, ndasunga chikhulupiriro.” (2 Timoteo 4:7)Ndani angasankhe mdani wawo woipitsitsa kukhala mneneri wawo?
Saulo (Paulo) ndi chitsanzo cha munthu amene sitingamusankhe kukhala olalikira uthenga wabwino, koma Yesu anamusankha. Zingatheke bwanji kuti anthu osayembekezereka nkukhala alaliki akulu (Mwamuna ogwidwa ziwanda, Mzimayi wa ku Samariya, hule, otolera misonkho, “osaphunzira” asodzi, opha akhristu…)?Chisomo cha mulungu chinasintha mitima yawo
. Ndipo anadzipereka kukauza ena za zozizwa zomwe Mulungu anachita miyoyo
yawo.
Paulo
sanasiye
kutsatira
cholinga
chake
kuyambira
pomwe anakomana ndi Yesu. Anapereka MOYO WAKE WONSE kulalikira
uthenga
wabwino
.
Slide6KUYAMBIRANSO ULENDO
“
Ananena
naye
kachitatu, ‘Simoni, mwana wa Yona, kodi undikonda ine?’ Petro anamva chisoni kuti anati kwa
iye kachitatu, ‘Kodi undikonda Ine?’ Ndipo anati kwa iye, ‘Ambuye, mudziwa inu zonse; muzindikira kuti ndikukondani inu
.’ Yesu ananena naye
, ‘Dyetsa
nkhosa
zanga.’” (
Yohane 21:17)
Petro anachita tchimo lalikulu
: Anamukana Yesu(Marko. 14:66-72). Anazimva kuti sangathe
kupitiriza kuudza ena za Yesu.
Koma
,
Yesu
anadziwa
mtima
wa
Petro,
Anadziwa
kuti
Petro
amamukondabe
. Nchifukwa chake
anamufunsa pagulu kuti avomereze za chikondi chake pa Iye
katatu
.
Yesu
anabwezeretsa
kudzidalira
kwa
Petro
ndi
kumupatsa
utumiki
:
Kuyangánira
mpingo wake
ndi
kulalikira
uthenga
wabwino
.
Kumene
kuli
kuonetsa chikondi chake mu ntchito
Mwina
mwamukanako
Yesu
kudzera
mu
ntchito
zanu
koposa
kamodzi
.
Nkhani
yabwino
ndiyakuti
chisomo
chikupezekabe
,
ndipo
mukungu
sanathane
nanu
. Malo
akadalipo
mu
ntchito
yake
ngati
muli
olola
.
Slide7NJIRA YA CHIKONDI
“
Umo
tizindikira
chikondi, popeza Iyeyu anapereka moyo wake chifukwa cha ife; ndipo ife tiyenera
kupereka moyo wathu chifukwa cha abale.” (1 Yohane 3:16)Yesu anamubwezeretsa Petro ndikulola kuti akhale nacho chisangalalo chachikulu mmoyo uno: Kuona miyoyo ikulowa mu ufumu wa Mulungu.Petro anaona zipatso zoyamba kuchokera mu
ulaliki wake pa tsiku la Pentecost (Machitidwe 2:14-41). Petro anasonyeza chikondi chomwe anachivomereza pa maso a Yesu
ndi ophunzira ake.
Petro
anayenera
kulipira
chikondi ndi chisangalalo chimenechi, mapeto ake
anataya moyo wake (Yohane 21:18-19).
Pambuyo pake Yohane analongosola kuti chikondi
chimaphatikizanso kuzipereka, nsembe yosazikonda, yosayembekezera mphoto
ina iriyonse.
Tsiku lomwe tidzakhale ndi Yesu ndi
opulumutsidwa
(
kuphatikiza
omwe
anamudziwa
Yesu chifukwa cha ife),
sitidzaonanso kanthu kamene tinachita pa dziko lino monga nsembe. Kutsatira Yesu
mpaka kumapeto kudzakhala
kokwanira
Slide8“Mzimu Woyera atatsika, pamene
ophunzira
anapita
kukalalika za mpulumutsi wa moyo, chokhumba chawo chachikulu chinali chipulumutso cha miyoyo. Anakondwera posonkhana ndi opulumutsidwa. Anali
okoma mtima, oganiza bwino, odziletsa,okonzeka kudzipereka chifukwa cha choonadi. Mukukhala kwawo tsiku ndi tsiku anaonetsera chikondi chomwe Khristu anachionetsa kwaiwo. Posanena kapena kuchita
modzikonda anayatsa chikondi mitima
ya ena”
E.G.W. (The Acts of the Apostles, cp. 54, p. 547)