/
UTUMIKI   WA  PETRO Phunziro 6 la pa August 11, 2018 UTUMIKI   WA  PETRO Phunziro 6 la pa August 11, 2018

UTUMIKI WA PETRO Phunziro 6 la pa August 11, 2018 - PowerPoint Presentation

moistbiker
moistbiker . @moistbiker
Follow
344 views
Uploaded On 2020-06-24

UTUMIKI WA PETRO Phunziro 6 la pa August 11, 2018 - PPT Presentation

Patangotsala pangono kuti Petro amukane Yesu anamuuza Petro kuti Ndipo iwe pamene watembenuka ukhazikitse abale ako Luka 2232 Petro adakwaniritsa ID: 785753

kwa ndi machitidwe petro ndi kwa petro machitidwe amitundu uthenga mulungu kuti ndipo wabwino mpingo utumiki ntchito yesu koma

Share:

Link:

Embed:

Download Presentation from below link

Download The PPT/PDF document "UTUMIKI WA PETRO Phunziro 6 la pa Aug..." is the property of its rightful owner. Permission is granted to download and print the materials on this web site for personal, non-commercial use only, and to display it on your personal computer provided you do not modify the materials and that you retain all copyright notices contained in the materials. By downloading content from our website, you accept the terms of this agreement.


Presentation Transcript

Slide1

UTUMIKI WA PETRO

Phunziro 6 la pa August 11, 2018

Slide2

Patangotsala pang’ono kuti Petro amukane, Yesu anamuuza Petro kuti “Ndipo iwe, pamene watembenuka ukhazikitse abale ako” Luka 22:32.Petro adakwaniritsa langizoli pozungulira ndi kularikira uthenga wabwino

malo

osiyanasiyana, kutumikira abale ake , anthu osowa, okaikakaika, komanso alendo okhalanawo mdziko.

Utumiki wa Petro.Utumiki wa machiritso. Machitidwe 9:32-43.Utumiki kwa amitundu. Machitidwe 10:1-43.Utumiki wa kuvomereza amitundu.Machitidwe 10:44-11:1-18.Utumiki wa mpingo.Kulalikira kwa amitundu. Machitidwe 11:19-30.Chisautso ndi kulondedwalondedwa kwa Ekelesia. Machitidwe 12.

Uthenga

udalalikidwanso kwa anthu amitundu okhala ku Antiyokeya.

Slide3

Machitidwe 9:32-43UTUMIKI WA MACHIRITSO

Ndipo Petro anagwira

dzanja lache , namnyamutsa ; ndipo m’mene adaitana oyera mtima ndi amasiye , anampereka iye wamoyo” (Machitidwe 9:41)Mulungu adagwiritsa ntchito Petro kuchita zozizwa zofanana

ndi zomwe Yesu Kristu adazichita.

Luka 5:17-26

Ndinena

kwa

iwe

,

Tauka

,

nusenze

kama wako numuke kunyumba kwako."

Machitidwe 9:32-35

“Eneya Yesu Kristu akuchilitsa iwe. Uka yalura mphasa yako”

Marko 5:35-43

“Komai Iye anawatulutsa onse ……… “ Buthu, ndinena ndi iwe, uka”

Machitidwe 9:36-43

Koma

Petro

anawaturutsa

onse

…………… “ Tabita,

uka

Slide4

Machitidwe 9:32-43Zotsatira za machiritso onsewa zinalizofanana; “ ambiri analemekeza Mulungu”, “ anthu anatembenukira kwa Ambuye” “ ambiri anakhulupilira

Ambuye” ndinso “ ambiri anagwidwa ndi kuzizwa kwakukulu”.

UTUMIKI WA MACHIRITSO“Ndipo Petro

anagwira dzanja lache

, namnyamutsa ; ndipo m’mene adaitana oyera

mtima

ndi

amasiye

,

anampereka

iye wamoyo” (

Machitidwe 9:41)

Pamene

talolera mwaphumphu kuti Mulungu Yehova atigwiritse ntchito mu utumiki wa uthenga wabwino,zazikulu zitha kuchitika.

Slide5

Ngero wa Yehova anamuuza Korneliyo amene ayenera

kumuitana

ndi kumalo kumene

munthuyo akupezeka.Kutengere pa kamvetsetsedwe ka nkhani ya chipulumutso pakati pa a Yuda, Petro monga muyuda weneweni otsata chilamulo, sadafuna kulowa

mnyumba ya munthu wa

amitundu.Chfukwa cha ichi

Mulungu

adagwiritsa

ntchito

masomphenya

apadera kumuuza Petro kuti

akalalikire uthenga wabwino

kwa amitundu.

Machitidwe 10:1-43UTUMIKI KWA AMITUNDU“Ndipo Petro anatsegula pakamwa pache

, nati

; Zoonadi ndizindikira kuti Mulungu alibe tsankhu.” (Machitidwe 10:34)

Yesu

Khristu adagwiritsa ntchito chitsanzo cha Petro kutiphunzitsa kuti chipulumutsa ndi cha aliyense

posayan’ganira mtundu

ndi

manenedwe

(Tito 2:11,

Agalatiya

3:26-28,

Aefeso

2:11-19).

Palibe

tsankho

,

chisomo

cha

Mulungu

chaperekedwa

kwa

onse

.

Kotero

tikuyenera

tilalikire

uthenga

wabwino

kwa

aliyense

.

Slide6

Machitidwe 10:44-11:1-18UTUMIKI WAKUVOMELEZA ACHIKUNJA“Ndipo pamene

anamva izi, anakhala du,

nalemekeza Mulungu, ndi kunene, Potero Mulungu anapatsa kwa amitundinso kutembenukira mtima ku moyo” (Machitidwe 11:18)Petro anaona amitundu akulandira Mzimu Oyera “ Monga anatero ife poyamba paja” Kotero anamvetsetsa

kuti amitunduwa atha kubatizidwa ndikukhala mbali

imodzi ya ziwalo za mpingo popanda m’dulidwe.Koma mpingo wa nthawi imeneyo sunali

okonzeka

kuwavomeleza

amitunduwa

kuti akhale mbali imodza ya ziwalo

za mpingo.Adatsutsana ndi chimene Petro adachita potengera uthenga kwa amitundu

. Koma pamene Petro adafotokoza nthano yonse ya momwe zidachitikira anthuwo adagonjera navomereza.

Khomo lidatseguka kwa amitundu. Ichi

chinabweretsa zotsatila zazikulu patsogolo pake.

Slide7

Machitidwe 11:19-30KULALIKIRA KWA AMITUNDU

Koma panali ena

mwa iwo, amuna a ku Kupro, ndi Kurene, amenewo, m’mene dafika ku Antiokeya, analamkhula ndi a Helene, ndikulalikila uthenga wabwino

wa Ambuye Yesu

Khristu”. (Machitidwe 11:20)Okhulupilira

ambiri

anathawa

ku

Yerusalem

chifukwa cha chisautso chachikulu

chotsogozedwa ndi Saulo. Adalalikira uthenga wabwino kwa muyuda aliyense adakomana naye. Ena

mwa iwo adaganiza zokalalikira uthenga kwa amitundu ku Antiokeya.Mulungu

adakonzetsera dongosolo lonse. Saulo adasandulika nakhala

mtumwi, Petro adayamba kulalikira uthenga kwa amitundu ndipo mpingo udawalandira amitunduwo.Pamene mpingo udamva kuti amitundu atembenuka mtima ku Antiokeya , udatumiza Barnaba “Chifukwa anali munthu wabwino, ndi odzala ndi mzimu oyera ndi chikhulupiliro”, amamudziwa Paulo, amadziwanso

kumalo komwe Paulo amapezeka.Barnaba ndi Paulo

analalikira limodzi uthenga wabwino ku Antiokeya kwa chaka chimodzi. Okhulupilira ku Antiokeya anatchedwa ‘ Akhristu” kwa nthawi yoyamba.

Slide8

Machitidwe 12KUZUNZIKA NDI KULONDEDWALONDEDWA

Koma nyengo

imeneyo Herod mfumu anathira manja ena a m, Ekelesia kuwachitira zoipa. Ndipo anapha ndi lupanga Yakobo mbale wa Yohane

” (Machitidwe 12:1-2)

Mdaniyo ( satana ) adakwiya ndi kukula kwa mpingo, nagwiritsa

ntchito

Herodi

pofuna

kuimitsa ntchito ya uthenga wabwino.

Imfa

ya

Yakobo

ndi kuikidwa mndende kwa Petro kudadandaulitsa mpingo.Herodi adayesetsa kuti Petro asathawe mundende chifukwa atumwi ena amatuluka mndende mosavuta. Machitidwe 5:17-20.Mpingo unakhala pamodzi ndi kupemphera, ndipo Mulungu adamva mapemphero

awo, natuma mngero wache namasula Petro mundende.

Herodi anavulazidwa ndi mngero wa Mulungu kumapeto kwake.

Slide9

“Kristu sadayang’ane kusiyana kwa mitundu, udindo ndi manenedwe. Alembi

ndi Afarisi adakhumba kupanga mphatso

yaulere ya kumwamba kukhala yawo yokha monga a Yuda, nasiya kunja ena onse opezeka padziko lapansi. Koma Yesu Khristu anadza kudzaphwasula makoma akugawikana. Anabwera

kudzaonetsa kuti monga mpweya, kuwala

, ndi mvura zitsitsimutsa dziko lapansi

popanda

kusankha

,

mphatso

yache

ya chifundo ndi chikondi yaperekedwa

kwa wina aliyense okhala pa

dziko lapansi. Moyo wa

Yesu Kristu udakhazikitsa chipembedzo chimene sichiona malire a mtundu wina ulionse, chipembedzo chimene ayuda ndi amitundu , mfulu ndi kapolo , ndi olumikizana mu ubale

umodzi , ofanana pamaso

pa Mulungu. Ndondomeko za mayendetsedwe adziko ( policy ) sizinatenge gawo pa mayendetsedwe a ntchito yake ya uthenga wabwino. Sadasiyanitse pakati pa

anansi ndi alendo

, abale ndi adani. Mtima wake nthawi zonse unakhudzika ndi miyoyo yodzala ndi ludzu la madzi amoyo”E.G.W. (The ministry of healing cp. 1,p 25)