8 August 22 2020 Kuunika kwa dziko lapansi Thandizo lokoma mtima Kupereka zosowa zawo Chinthu chofunika kwambiri Zofunikira kwa Yesu Yesu anachita ID: 813186
Download The PPT/PDF document "KUTUMIKIRA MONGA YESU Phunziro" is the property of its rightful owner. Permission is granted to download and print the materials on this web site for personal, non-commercial use only, and to display it on your personal computer provided you do not modify the materials and that you retain all copyright notices contained in the materials. By downloading content from our website, you accept the terms of this agreement.
Slide1
KUTUMIKIRA MONGA YESU
Phunziro
8,
August
22, 2020
Slide2Kuunika kwa dziko lapansiThandizo lokoma mtimaKupereka zosowa
zawoChinthu chofunika kwambiriZofunikira kwa Yesu
Yesu anachita zambiri
pambali pa kulalikira za ufumu wa kumwamba
. Ankakhala pamodzi ndi anthu, kumvetsera
zonena zawo, komanso kuwachitira zabwino
.Yesu anawathandiza m’mavuto pnse amene anadza nawo kwa
iye.Iye ali chitsanzo
chathu
pamene tikutumikira.
Slide3KUUNIKA KWA DZIKO LAPANSI
“Pamenepo Yesu
analankhulanso nao
, nanena,
Ine
ndine kuunika
kwa dziko
lapansi;
iye
wonditsata
Ine sadzayenda
mumdima, koma adzakhala
nako
kuunika
kwa moyo
.’”
(
Yohane
8:12)
Yesu anabwera pa dziko lapansi kudzachotsa mdima wa uchimo ndi kuunika kwa chipulumutso (Yohane 1:4-5; 3:19-21).
Khalani Mchere. Mchere ukuyenera kusakanizika ndi chakudya kuti ulowerere ndi kukometsa chakudyacho. Tikuyenera tikhala mu dziko lapansi kuti uthenga wabwino ulowere bwino (Yohane 17:15-18).Khalani Kuunika. Kuwala kupezeka mumdima omwe ukupezeka ku malo omwe timakhala, mmidzi, ndi mmizinda, kuwaunika ndi kuwala kwa ulemerero wa mulungu (Afilipi 2:15).
Anakhala pakati pa anthu kuti akwaniritse izi. “Anali kuchitira anthu za bwino ndi kuchiritsa onse” (Machitidwe 10:38).
Anatilimbitsa
ife
kumutsatira
kupyolera
mu
zitsanzo
ziwiri
izi
(
Mateyu
5:13-14):
Slide4“Sicholinga cha Mulungu kuti tidzipatule
ku dziko lapansi. Koma kuti
pamene tikadali
mudziko lapansi
tidzipatule tokha kwa
Mulungu. Sitiyenera
kutsatira zochitika za dziko lapansi
. Tikuyenera kukhala
mudziko
lapansi
monga zokometsera, monga mmene
mchere umasunga kukoma kwake.
Pakati pa anthu
ochimwa, odetsedwa,
opembedza mafano, tiyenera
kukhala oyera
,
kusonyeza
kuti mu chisomo cha Khristu
yakubwerezeretsa chiyero mwa munthu. Tikuyenera kuonetsera mphamvu ya kupulumutsa ku dziko lapansi.”E.G.W. (Counsels on Health, p. 592)
Slide5THANDIZO LOKOMA MTIMA“
Mau anu akhale mçhisomo
, okoleretsera,
kuti mukadziwe
inu mayankhidwe
anu a
kwa yense akatani.
” (Akolose
4:6)
Yesu
anapeze ndi kuonetsera mankhalidwe abwino mwa ena (Mateyu
8:10; Marko 12:34).Chotero, mitima yawo inali yomatseguka kulandira mau a Yesu
.Yesu anali okoma mtima
kwambiri kotero kuti anali kusamalitsa
kuti asadzudzule mokhumudwitsa iwo omwe
anali atangokhulupirira. Yesu anali okoma
mtima
kwambiri kotero amakhutitsa ka chikhulupiriro kakangóno nkati mwa
mitima yawo (Yesaya 42:3).Tiyambe tapeza zinthu zabwino mwa amene atizungulira ndipo tiwaonetse anthu za ubwino wawo
. Mu njira iyi tidzakhudza miyoyo yawo mwapadera.
Slide6KUPEREKA ZOSOWA ZAWO
” Ndipo onani,
anabwera naye
kwa Iye
munthu wamanjenje
, wakugona pamphasa
: ndipo Yesu pakuona
chikhulupiriro chao,
anati
kwa
wodwalayo, Limba mtima,
mwana, machimo ako akhululukidwa
.(Matthew 9:2)
Yesu anazindikira
zosowa za ena ndipo anabwezeretsa
ku thupi, m’malingaliro, m’maganizo komanso
muuzimu
.
Amathetsa mavuto awo ndikuwaitanira kuti afunefune moyo wa
muyaya : “Machimo ako akhululukidwa”; “Chikhulupiriro chako chakupulumutsa iwe”; “Pita usakachimwenso.” (Mateyu 9:2; Luka 8:48; Yohane 8:11)Tiyenera kukwaniritsa zosowa za ena ndikuyesera kukwaniritsa ngati
tingathe.Pamene tikwaniritsa zosowa zawo, timatsegulanso khomo kuwaonetsera mmene angakwaniritsire chosoweka chachikulu kwa aliyense (ngakhale asakudziwa): Kumasulidwa ku uchimo, moyo osatha; amene ali, Yesu.
Slide7CHINTHU CHOFUNIKA KWAMBIRI“Ndipo
Yesu anayendayenda m'mizinda
yonse ndi
m'midzi, namaphunzitsa
m'masunagoge
mwao, nalalikira
Uthenga Wabwino wa
Ufumuwo, nachiritsa
nthenda
iliyonse ndi zofooka zonse
.”(
Mateyu 9:35)
Utumiki
wa Yesu
unakhazikika
pa ngodya
zitatu:Kodi ngodya yopambana kwambiri kwa Yesu inali
iti? (Marko 1:38)Iye anabwera pa dziko lapansi “kufunafuna ndi kupulumutsa chotaikacho.” (Luka 19:10). Chotero, kulalikira za chipulumutso ndi kuphunzitsa ena kunali kopambana kwambiri.Pambali pa ichi, kuchiza inali njira yoonetsera khalidwe leni leni la Mulungu komanso kupereka moyo wosatha.
Slide8ZOFUNIKA KWA YESU
“
‘Pakuti ndidzakubwezera
iwe
moyo, ndipo
ndidzapoletsa mabala
ako, ati Yehova
,’”
(
Yeremiya
30:17)
Mulungu
anagwiritsa ntchito aneneri kuyankhula za nthenda yosachiritsidwa : Tchimo (Yesaya 1:5;
Yeremiya 30:12).Yesu akufunitsitsa aliyense
achiritsidwe ku nthenda imeneyi, ndikuona
omwe achiritsidwa kale akubweretsa machiritso kwa
ena.
Yesu
anagwiritsa
ntchito mafanizo atatu kunena za masiku otsiriza mu buku la Mateyu 25. Amatilimbikitsa kuti tidzadzidwe ndi Mzimu Woyera and kugwiritsa ntchito mphatso
zomwe zapatsidwa kwa ife mokhulupirika.Mufanizo lomalizira anafotokoza za makhalidwe a akhristu owona. Amene akhala moyo otumikira ena osati odzikonda adzalandiridwa kwa Iye.
Slide9“Chisomo cha Khristu chomwe
chaululiridwa kwa ife chiyenera kuuluridwa
kwa ena
mwa chikondi.
Chisoni komanso chifundo
chachikulu chizadzadza
miyoyo ya iwo omwe
akadali m’manja
mwa
Satana
. Khristu akuyenera kuchulukitsidwa mwa
amuna ndi akazi onse
omwe amukhulupirira
Iye, chifukwa akuyenera
kukhala mmoyo
wa Khristu pa
kudalitsa
,
kuunikira komanso kubweretsa
chiyembekezo, mtendere ndi Chimwemwe m’mtima ya ena.”E.G.W. (Our Father Cares, May 20)