/
KUONA ANTHU KUPYOLERA MMASO A YESU KUONA ANTHU KUPYOLERA MMASO A YESU

KUONA ANTHU KUPYOLERA MMASO A YESU - PowerPoint Presentation

backbays
backbays . @backbays
Follow
342 views
Uploaded On 2020-10-22

KUONA ANTHU KUPYOLERA MMASO A YESU - PPT Presentation

Lesson 3 for July 18 2020 Kutsogolera Ena Kulandira Aliyense Kupanga Maubwenzi Kuchitira ena za bwino Kugwiritsa Ntchito Mwai Uliwonse Kodi Yesu ankaona ID: 815178

yesu ndi ena anthu ndi yesu anthu ena ndipo iye kuti kwa ntchito mulungu munthu yohane aliyense kuona mwai

Share:

Link:

Embed:

Download Presentation from below link

Download The PPT/PDF document "KUONA ANTHU KUPYOLERA MMASO A YESU" is the property of its rightful owner. Permission is granted to download and print the materials on this web site for personal, non-commercial use only, and to display it on your personal computer provided you do not modify the materials and that you retain all copyright notices contained in the materials. By downloading content from our website, you accept the terms of this agreement.


Presentation Transcript

Slide1

KUONA ANTHU KUPYOLERA MMASO A YESU

Lesson 3 for July 18, 2020

Slide2

Kutsogolera

Ena

Kulandira AliyenseKupanga MaubwenziKuchitira ena za bwinoKugwiritsa Ntchito Mwai Uliwonse

Kodi Yesu ankaona anthu motani?Ankawachitira chifundo. Ankaganizira kuti moyo uli wonse tiofunika kupulumuka. Ankaona munthu mmene angasinthira atalandira chipulumutso.Munthu aliye anali wafunika ndi wapadera kwa Yesu. Kotero, samanyoza aliyense koma ankamuona aliyense mwa njira yapadera. Tiyeni tiphunzire kuona anzathu mmene Yesu akanawaonera.

Slide3

KUTSOGOLERA ENA

Ndipo

anadza ku Betsaida. Ndipo anadza naye kwa Iye munthu wakhungu, nampempha Iye kuti amkhudze.”

(Marko 8:22)Ichi chinali chozizwitsa chapadera m’njira za mbiri.

1. Anthu ena, anabwera

ndi nzawo wakhungu, napempha kuti

Yesu amuchize

2. Yesu anamutengera

pambali

3.

Atamukhudza

koyamba

,

anamufunsa

ngati

akuona

kanthu

4.

Wakhunguyu anaona anthu ngati mitengo

5. Atakhudzidwa kachiwiri, anachira kwathuthu

Slide4

KULANDIRA ALIYENSE

Ndipo

anayenera kupita pakati pa Samariya.” (Yohane 4:4)Ubale wapakati pa a Yuda ndi a Samaliya unali oteketseka. Ayuda pochoka ku Yudea kupita ku Galileya ankazungulira mzinda

wa Samaliya posafunina kudutsamo.GalileyaSamaliyaYudeaPamene tiona ena ndi chifundo cha Mulungu, matchinga onse amaphwasulidwa

. Sipakhalanso kusiyana, chifukwa aliyense timamuona oyenera kulowa mu ufumu wa

kumwambaSitikuyera kugwirizana nawo

mmaganizo awo a ndale kapena chipembedzo

, Koma timawakonda ndipo timawafunira zabwino

.

Koma

,

Yesu

amaona

kupyola

,

mtundu

,

chikhalidwe

,

chibadidwe

komanso chipembedzo. Ankadziwa kuti ku

Samaliyanso kunali anthu ofunika chipulumutso,ndipo inali ntchito yake kuwapititsira chipulumutso.

Slide5

KUPANGA MA UBWENZI

Anayamba

iye kupeza mbale wake yekha Simoni, nanena naye, Tapeza ife Mesiya (ndiko kusandulika Khristu).”

(Yohane 1:41)Pamene Yesu ankatsanzika ophunzira ake, anawapempha alalikira uthenga wabwino kumadera ambiri: “Ku Yerusalemu, konse ku Yudea ndi Samaliya, ndi kumapeto a dziko.” (Machitidwe 1:8).

Ntumwi Andrea anapereka

chitsanzo chabwino. Koyamba, Anauza nchimwene

wake za Yesu[Yudea].Kenaka anapanga

ubwenzi ndi ka nyamata[Samaliya] nachita

zozizwa kuopyolera mwa iye (

Yohane

6:5-11).

Pambuyo

pake

anagawa

uthenga

wabwino

kwa

alendo [kumapeto a dziko], monga a Giriki amene ankafuna kudziwa za

Yesu(Yohane 12:20-26).Tingathe kuphunzira kagwiridwe ka ntchito

yokopa anthu kuchokora kwa Andrea: Kupanga ma ubwenzi

/ubale ndi ena.

Slide6

KUCHITIRA ENA ZABWINO

Ndipo

pakuona kuti anayankha ndi nzeru, Yesu anati kwa iye, Suli kutali ndi

Ufumu wa Mulungu. Ndipo palibe munthu analimbanso mtima kumfunsa Iye kanthu.” (Marko 12:34)Kodi Yesu

anachita nawo bwanji anthu ovuta?

Kuona

anthu ena

m’maso a Yesu zikutathauza kuona ena

kuti ndi mbadwa za ufumu wa

kumwamba,ndi

kuchita

nawo

moyenera

.

Kuti

tipindule

ndi umboni

wathu, tikuyenera kupempha Mzimu Woyera ativumbulutsire chinsinsi ichi.

Slide7

KUGWIRITSA NTCHITO MWAI ONSE OPEZEKA

Ndidziwa

ntchito zako (taona, ndapatsa pamaso pako khomo lotseguka limene munthu sangathe kutsekapo), kuti uli nayo

mphamvu pang'ono, ndipo unasunga mau anga, osakana dzina langa.” (Chivumbulutso 3:8)Mulungu amatsegula makomo kutipatsa mwai oti

tiperekere umboni.Mwachitsanzo Filipi: Mulungu anamuika pa malo

oti akumane ndi munthu yemwe

ankawerenga malemba a nchipangano chakale. Munthuyu

ankangofunika kuthandizidwa pangóno kuti apereke

moyo wake kwa Yesu(Acts 8:26-39).Pali

angelo

osaoneka

ndi

maso

anthu

omwe

ndiokozeka kutionetsa

iwo amene angatsegule makomo awo kulandira mawo a Mulungu. Pemphani Mulungu akupatseni

masomphenya ozindikira mwai opezeka komanso mawo oyenera kugawana ndi ena

Slide8

“Yesu anakhala yekha

pakati

pa anthu. Sanazipatule kwa iwo amene anafuna chithandizo kuchokera kwa iye. Analowa nyumba za anthu, ku khudza olira, kuchidza odwala, kudzudzula olakwitsa, ndi

kuchita ntchito za bwino. Ndipo ngati tikutsata mapazi a Yesu, tichite momwe anachitira iye. Tithandize ena monga mmene iye anachitira.”E.G.W. (Our Father Cares, February 17)